^
LUKA
Mawu Oyamba
Aneneratu za Kubadwa kwa Yohane Mʼbatizi
Aneneratu za Kubadwa kwa Yesu
Mariya Acheza kwa Elizabeti
Nyimbo ya Mariya
Kubadwa kwa Yohane Mʼbatizi
Nyimbo ya Zakariya
Kubadwa kwa Yesu
Abusa ndi Angelo
Yesu Aperekedwa mʼNyumba ya Mulungu
Yesu mʼNyumba ya Mulungu
Yohane Mʼbatizi Akonza Njira
Ubatizo wa Yesu
Makolo a Yesu
Kuyesedwa kwa Yesu
Yesu Akanidwa ku Nazareti
Yesu Atulutsa Mzimu Woyipa
Yesu Achiritsa Anthu Ambiri
Yesu Ayitana Ophunzira Oyamba
Yesu Achiritsa Munthu Wakhate
Yesu Achiritsa Wofa Ziwalo
Kuyitanidwa kwa Levi
Yesu Afunsidwa za Kusala Kudya
Yesu Mbuye wa Sabata
Atumwi Khumi ndi Awiri
Madalitso ndi Tsoka
Kukonda Adani
Za Kuweruza Ena
Mtengo ndi Zipatso Zake
Womanga Nyumba Wanzeru ndi Wopusa
Chikhulupiriro cha Kenturiyo
Yesu Aukitsa Mwana wa Mayi Wamasiye
Yesu ndi Yohane Mʼbatizi
Yesu Adzozedwa ndi Mayi Wochimwa
Fanizo la Wofesa
Nyale ndi Choyikapo Chake
Amayi ndi Abale a Yesu
Yesu Aletsa Namondwe
Achiritsidwa Munthu Wogwidwa ndi Ziwanda
Mwana Wamkazi wa Yairo ndi Mayi Wokhudza Chovala cha Yesu
Yesu Atuma Ophunzira ake Khumi ndi Awiri
Yesu Adyetsa Anthu 5,000
Petro Avomereza Khristu
Yesu Aneneratu za Imfa yake
Maonekedwe a Ulemerero wa Yesu pa Phiri
Kuchiritsidwa kwa Mwana Wogwidwa ndi Chiwanda
Yesu Abwereza Kunena za Imfa yake
Wamkulu Ndani?
A Samariya Akana Yesu
Kutsatira Yesu
Yesu Atuma Ophunzira 72
Fanizo la Msamariya Wachifundo
Marita ndi Mariya
Yesu Aphunzitsa za ku Pemphera
Yesu ndi Belezebabu
Za Mzimu Woyipa
Munthu Wodala
Chizindikiro cha Yona
Nyale ndi Thupi
Tsoka la Afarisi ndi Alembi Amalamulo
Chenjezo ndi Chilimbikitso
Fanizo la Munthu Wachuma Wopusa
Musadere Nkhawa
Chuma cha Kumwamba
Kukhala a Atcheru
Wantchito Wokhulupirika ndi Wosakhulupirika
Za Kugawikana
Kumasulira Nthawi
Za Kutembenuka Mtima
Mayi Wokhota Msana Achiritsidwa pa Sabata
Fanizo la Mbewu ya Mpiru ndi la Yisiti
Khomo Lopapatiza
Yesu Amvera Chisoni Yerusalemu
Yesu Mʼnyumba ya Mfarisi
Kudzichepetsa ndi Kulandira Ulemu
Fanizo la Phwando Lalikulu
Dipo la Kutsatira Yesu
Fanizo la Nkhosa Yotayika
Fanizo la Ndalama Yotayika
Fanizo la Mwana Wolowerera
Fanizo la Kapitawo Wosakhulupirika
Ziphunzitso Zina
Za Munthu Wachuma ndi Lazaro
Za Uchimo, Chikhulupiriro ndi Ntchito
Yesu Achiritsa Akhate Khumi
Za Ufumu wa Mulungu
Fanizo la Mayi Wakhama pa Kupempha
Fanizo la Mfarisi ndi Wolandira Msonkho
Yesu Adalitsa Ana Aangʼono
Munthu Wachuma ndi Ufumu wa Mulungu
Yesu Aneneratu za Imfa Yake Kachitatu
Yesu Achiritsa Wosaona
Zakeyu Apulumutsidwa
Antchito Opindula Mosiyana
Yesu Alowa mu Yerusalemu Mwaulemerero
Yesu mʼNyumba ya Mulungu
Amufunsa Yesu za Ulamuliro Wake
Fanizo la Olima Mʼmunda Wamphesa
Za Kupereka Msonkho kwa Kaisara
Za Kuuka kwa Akufa ndi Ukwati
Khristu ndi Mwana wa Ndani?
Achenjeza za Aphunzitsi Amalamulo
Chopereka cha Mayi Wamasiye
Zizindikiro za Masiku Otsiriza
Kuwonongedwa kwa Yerusalemu
Fanizo la Mtengo Wamkuyu
Za Kukhala Tcheru
Yudasi Avomera Kumupereka Yesu
Paska Womaliza
Za Mgonero wa Ambuye
Mkangano Pakati pa Ophunzira
Yesu Aneneratu kuti Petro Adzamukana
Yesu Apemphera ku Phiri la Olivi
Amugwira Yesu
Petro Akana Yesu
Asilikali Amuchita Chipongwe Yesu
Yesu Pamaso pa Pilato ndi Herode
Kupachikidwa kwa Yesu
Imfa ya Yesu
Yesu Ayikidwa Mʼmanda
Yesu Auka kwa Akufa
Zochitika pa Njira ya ku Emau
Yesu Aonekera kwa Ophunzira
Kupita Kumwamba