^
MACHITIDWE A ATUMWI
Lonjezo la Mzimu Woyera
Yesu Akwera Kumwamba
Matiyasi Alowa Mʼmalo mwa Yudasi Isikarioti
Kubwera kwa Mzimu Woyera
Uthenga wa Petro
Kuyanjana kwa Okhulupirira
Petro Achiritsa Wolumala Miyendo
Petro Ayankhula kwa Anthu
Petro ndi Yohane ku Bwalo la Akulu
Okhulupirira Apemphera
Okhulupirira Agawana Zinthu Zawo
Hananiya ndi Safira
Atumwi Achiritsa Anthu Ambiri
Atumwi Azunzidwa
Asankha Atumiki Asanu ndi Awiri
Ayuda Agwira Stefano
Mawu a Stefano
Kuphedwa kwa Stefano
Kuzunzika kwa Mpingo
Filipo ku Samariya
Simoni Wamatsenga
Filipo ndi Nduna ya Zachuma ya ku Etiopia
Kutembenuka Mtima kwa Saulo
Saulo Alalikira ku Damasiko
Saulo ku Yerusalemu
Eneya ndi Tabita
Kenturiyo Korneliyo Ayitana Petro
Masomphenya a Petro
Petro ku Nyumba ya Korneliyo
Petro Afotokozera Mpingo
Mpingo wa ku Antiokeya
Petro Apulumuka Mʼndende
Imfa ya Herode
Barnaba ndi Saulo Atumidwa ndi Mpingo
Ku Kupro
Antiokeya wa ku Pisidiya
Ku Ikoniya
Ku Lusitra ndi ku Derbe
Paulo ndi Barnaba Abwerera ku Antiokeya wa ku Siriya
Msonkhano wa ku Yerusalemu
Kalata Yopita kwa Anthu a Mitundu ina
Paulo Asiyana ndi Barnaba
Timoteyo Atsagana ndi Paulo ndi Sila
Paulo Awona Masomphenya
Lidia Atembenuka Mtima ku Filipi
Paulo ndi Sila Mʼndende
Paulo ku Tesalonika
Ku Bereya
Ku Atene
Ku Korinto
Prisila, Akula ndi Apolo
Za Apolo
Paulo ku Efeso
Za Ana a Skeva
Chipolowe ku Efeso
Paulo Apita ku Makedoniya ndi ku Grisi
Paulo Aukitsa Utiko ku Trowa
Paulo Alawirana ndi Akulu Ampingo a ku Efeso
Paulo Apita ku Yerusalemu
Paulo Afika ku Yerusalemu
Agwira Paulo
Paulo Ayankhula
Paulo Nzika ya Chiroma
Paulo ku Bwalo Lalikulu la Ayuda
Ayuda Achita Chiwembu Paulo
Paulo Apita ku Kaisareya
Felike Amva Mlandu wa Paulo
Paulo ku Bwalo la Milandu la Festo
Festo Afotokozera Mfumu Agripa
Paulo Pamaso pa Agripa
Mawu a Paulo Pamaso pa Mfumu Agripa
Paulo Apita ku Roma
Namondwe pa Nyanja
Kuwonongeka kwa Sitima
Paulo pa Chilumba cha Melita
Paulo Afika ku Roma
Paulo Alalikira kwa Ayuda ku Roma