^
DEUTERONOMO
Mose Akumbutsa Aisraeli za ku Horebu
Kukhazikitsa Atsogoleri
Atumizidwa Kukazonda Dziko
Awukira Yehova
Kuyendayenda Mʼchipululu
Kugonjetsedwa kwa Sihoni Mfumu ya ku Hesiboni
Kugonjetsedwa kwa Ogi Mfumu ya ku Basani
Kugawana Dziko
Mose Aletsedwa Kuwoloka Yorodani
Alamulidwa Kukhala Womvera
Mafano Aletsedwa
Yehova Ndiye Mulungu
Mizinda Yothawirako
Kufotokozera za Malamulo
Malamulo Khumi
Konda Yehova Mulungu Wako
Apirikitsa Mitundu Ina ya Anthu
Musayiwale Yehova
Osati Chifukwa cha Kulungama kwa Israeli
Mwana Wangʼombe Wagolide
Miyala Ngati Yoyamba Ija
Kuopa Yehova
Kukonda ndi Kumvera Yehova
Malo Amodzi Opembedzera
Kupembedza Milungu Ina
Zoletsedwa pa Maliro
Za Chakhumi
Chaka Chokhululukira Ngongole
Kumasula Akapolo a Chihebri
Ziweto Zoyamba Kubadwa
Paska
Chikondwerero cha Masabata
Chikondwerero cha Misasa
Oweruza
Kupembedza Milungu Ina
Mabwalo a Milandu
Mfumu
Zopereka za kwa Ansembe ndi Alevi
Makhalidwe Oletsedwa
Aneneri
Mizinda Yothawirako
Mboni
Za ku Nkhondo
Nsembe Yopepesera Munthu Akaphedwa Mosadziwika Bwino
Kukwatira Mkazi Wogwidwa ku Nkhondo
Ufulu wa Mwana Woyamba Kubadwa
Mwana Wamwamuna Wowukira
Malamulo Osiyanasiyana
Malamulo a Ukwati
Wosayenera mu Msonkhano
Masamalidwe a Msasa
Malamulo Osiyanasiyana
Zipatso Zoyamba ndi Chakhumi
Tsatirani Malamulo a Yehova
Guwa Lansembe ku Phiri la Ebala
Matemberero Kuchokera ku Phiri la Ebala
Madalitso Akumvera
Matemberero Akusamvera
Kukonzanso Pangano
Madalitso Akabwerera kwa Yehova
Moyo kapena Imfa
Yoswa Alowa Mʼmalo mwa Mose
Kuwerenga Malamulo
Aneneratu za Kuwukira kwa Aisraeli
Nyimbo ya Mose
Mose Adzafera pa Phiri la Nebo
Mose Adalitsa Mafuko a Aisraeli
Mose Amwalira