^
EKSODO
Aisraeli Azunzidwa ku Igupto
Azamba Akana Kumvera Mfumu
Kubadwa kwa Mose
Mose Athawira ku Midiyani
Kuyitanidwa kwa Mose pa Chitsamba Choyaka Moto
Mulungu Apatsa Mose Mphamvu Zochita Zodabwitsa
Mose Abwerera ku Igupto
Mose Akumana ndi Farao
Njerwa Zopanda Udzu
Mulungu Alonjeza Chipulumutso
Mibado ya Mose ndi Aaroni
Aaroni Ayankhula Mʼmalo mwa Mose
Ndodo ya Aaroni Isanduka Njoka
Mliri wa Magazi
Mliri wa Achule
Mliri wa Nsabwe
Mliri wa Ntchentche Zoluma
Mliri pa Ziweto
Mliri wa Zotupa
Mliri wa Mvula ya Matalala
Mliri wa Dzombe
Mliri wa Mdima
Mliri wa Imfa ya Ana Oyamba Kubadwa
Kukhazikitsidwa kwa Paska
Kutuluka kwa Aisraeli
Lamulo la Paska
Mwambo Wopatula Ana Oyamba Kubadwa
Kuwoloka Nyanja
Nyimbo ya Mose ndi Miriamu
Madzi a ku Mara ndi Elimu
Mana ndi Zinziri
Madzi Otuluka Mʼthanthwe
Aisraeli Agonjetsa Aamaleki
Yetero Abwera Kudzaona Mose
Pa Phiri la Sinai
Malamulo Khumi
Za Mafano ndi Maguwa Ansembe
Antchito a Chihebri
Munthu Akapwetekedwa
Za Kuteteza Katundu
Malamulo a Kakhalidwe ka Anthu
Malamulo a Zachilungamo ndi Zachifundo
Malamulo a Nthawi Zopuma
Masiku Atatu Akulu a Chikondwerero
Kutsogolera kwa Mngelo wa Mulungu
Kutsimikizira kwa Pangano
Zopereka Zomangira Chihema
Bokosi la Chipangano
Tebulo la Buledi Woperekedwa kwa Mulungu
Choyikapo Nyale
Chihema cha Mapemphero
Guwa Lansembe Yopsereza
Za Bwalo la Chihema
Mafuta Anyale
Zovala za Ansembe
Efodi
Chovala Chapachifuwa
Zovala Zina za Ansembe
Mwambo Wopatula Ansembe
Guwa Lansembe Yofukiza
Za Chopereka Chowombolera Moyo
Za Beseni Losambira
Mafuta Wodzozera
Za Zofukiza
Bezaleli ndi Oholiabu
Za Sabata
Za Fano la Mwana Wangʼombe Wagolide
Tenti ya Msonkhano
Mose ndi Ulemerero wa Yehova
Miyala ina Yatsopano
Nkhope ya Mose Inyezimira
Malamulo Osunga Sabata
Zopereka ku Malo Opatulika
Bezaleli ndi Oholiabu
Chihema
Bokosi la Chipangano
Mapangidwe a Tebulo
Mapangidwe a Choyikapo Nyale
Guwa Lofukizirapo Lubani
Guwa Lansembe Yopsereza
Beseni Losambira
Bwalo la Chihema
Zipangizo Zachitsulo za ku Malo Opatulika
Zovala za Ansembe
Chovala cha Efodi
Chovala Chapachifuwa
Zovala zina za Unsembe
Mose Ayendera Chihema
Adzutsa Chihema
Ulemerero wa Yehova