^
YOHANE
Mawu Asandulika Thupi
Yohane Mʼbatizi Akana kuti Iye ndi Khristu
Yesu Mwana Wankhosa wa Mulungu
Ophunzira Oyamba a Yesu
Yesu Ayitana Filipo ndi Natanieli
Yesu Asandutsa Madzi Kukhala Vinyo
Yesu Ayeretsa Nyumba ya Mulungu
Yesu Aphunzitsa Nekodimo za Kubadwa Kwatsopano
Yohane Mʼbatizi Achita Umboni za Yesu
Yesu Acheza ndi Mayi wa ku Samariya
Ophunzira Abweranso kwa Yesu
Asamariya Ambiri Akhulupirira
Yesu Achiritsa Mwana wa Nduna ya Mfumu
Yesu Achiritsa Munthu pa Sabata
Yesu Adziwulula kuti ndi Mwana wa Mulungu
Maumboni Onena za Yesu
Yesu Adyetsa Anthu 5,000
Yesu Ayenda pa Madzi
Yesu Chakudya Chamoyo
Ophunzira Ambiri Aleka Kutsata Yesu
Yesu Apita Kuphwando Lamisasa
Yesu Aphunzitsa pa Phwando
Kodi Yesu ndi Khristu?
Mitsinje ya Madzi Opatsa Moyo
Kusakhulupirira kwa Atsogoleri a Ayuda
[Mipukutu yoyambirira ndi maumboni akale mulibe 7:53 mpaka 8:11]
Za Mkazi Wachigololo
Za Umboni wa Yesu
Mkangano Woti Yesu Ndani
Ana a Abrahamu
Ana a Mdierekezi
Zomwe Yesu Ananena za lye Mwini
Yesu Achiritsa Munthu Wosaona Chibadwire
Afarisi Afufuza za Kuchiritsidwa Kwake
Kusaona kwa Uzimu
Mʼbusa Wabwino ndi Nkhosa Zake
Kusakhulupirira kwa Ayuda
Imfa ndi Kuukitsidwa kwa Lazaro
Yesu Atonthoza Alongo a Lazaro
Yesu Aukitsa Lazaro
Ayuda Apangana za Kupha Yesu
Mariya Adzoza Mapazi a Yesu
Yesu Alowa mu Yerusalemu
Agriki Afuna Kuona Yesu
Ayuda Apitirira Kusakhulupirira
Yesu Asambitsa Mapazi a Ophunzira Ake
Yesu Aneneratu za Kuperekedwa Kwake
Yesu Aneneratu za Kuperekedwa Kwake
Yesu Aneneratu kuti Petro Adzamukana
Yesu Atonthoza Ophunzira Ake
Yesu Njira ya kwa Atate
Lonjezo la Mzimu Woyera
Mpesa ndi Nthambi
Dziko Lapansi Limada Ophunzira a Yesu
Ntchito ya Mzimu Woyera
Ntchito ya Mzimu Woyera
Chisoni cha Ophunzira Chisandulika Chimwemwe
Yesu Adzipempherera Yekha
Yesu Apempherera Ophunzira Ake
Yesu Apempherera Okhulupirira Onse
Amugwira Yesu
Amutengera Yesu kwa Anasi
Petro Akana Yesu Koyamba
Mkulu wa Ansembe Amufunsa Yesu
Petro Akana Yesu Kachiwiri ndi Kachitatu
Yesu ku Bwalo la Pilato
Yesu Aweruzidwa kuti Aphedwe
Kupachikidwa kwa Yesu
Imfa ya Yesu
Yesu Ayikidwa Mʼmanda
Yesu Auka kwa Akufa
Yesu Aonekera kwa Mariya wa ku Magadala
Yesu Aonekera kwa Ophunzira ake Tomasi Palibe
Yesu Aonekera kwa Tomasi
Cholinga cha Uthenga Wabwino wa Yohane
Yesu Aonekera kwa Ophunzira ku Nyanja ya Tiberiya
Yesu Abwezeretsa Petro