^
MATEYU
Makolo a Yesu Khristu Monga mwa Thupi
Kubadwa kwa Yesu Khristu
Anzeru a Kummawa
Athawira ku Igupto
Kuphedwa kwa Ana mʼBetelehemu
Abwerera ku Nazareti
Yohane Mʼbatizi
Kubatizidwa kwa Yesu
Yesu Ayesedwa Mʼchipululu
Yesu Ayamba Kulalikira
Yesu Ayitana Ophunzira ake Oyamba
Yesu Achiritsa Odwala
Chiphunzitso cha pa Phiri
Mchere ndi Kuwunika
Kukwaniritsa Malamulo
Zokhudza Kupha
Zokhudza Chigololo
Zokhudza Kusudzula Mkazi
Malonjezo
Za Kubwezera Choyipa
Kukonda Adani
Zopereka Zachifundo
Za Kupemphera
Kusala Kudya
Za Chuma cha Kumwamba
Diso Nyale ya Thupi
Musade Nkhawa
Za Kuweruza Ena
Pemphani, Funafunani, Gogodani
Zipata Ziwiri ndi Njira Ziwiri
Aneneri Owona ndi Onyenga
Ophunzira Owona ndi Onyenga
Womanga Nyumba Wanzeru ndi Wopusa
Yesu Achiritsa Wakhate
Chikhulupiriro cha Kenturiyo
Yesu Achiritsa Anthu Ambiri
Za Kutsatira Yesu
Yesu Aletsa Namondwe
Ogwidwa ndi Ziwanda a ku Gadara
Munthu Wakufa Ziwalo wa ku Kaperenawo
Kuyitanidwa kwa Mateyu
Za Kusala Kudya
Za Mwana Wamkazi wa Yairo ndi Mayi Wokhudza Chovala cha Yesu
Yesu Achiritsa Osaona ndi Osayankhula
Antchito ndi Ochepa
Yesu Atuma Ophunzira Ake
Otumidwa ndi Yohane Mʼbatizi
Tsoka la Mizinda Itatu Yosatembenuka mtima
Goli la Khristu
Yesu Mbuye wa Sabata
Yesu Achiritsa Munthu Wolumala Dzanja
Mtumiki Wosankhidwa ndi Mulungu
Mwano wa Afarisi
Mtengo ndi Zipatso Zake
Chizindikiro cha Yona
Za Mzimu Woyipa
Amayi ndi Abale Ake a Yesu
Fanizo la Wofesa Mbewu
Tanthauzo la Fanizo la Wofesa
Fanizo la Namsongole
Fanizo la Mbewu ya Mpiru ndi Yisiti
Yesu Awatanthauzira Fanizo la Namsongole
Fanizo la Chuma Chobisika ndi la Ngale
Fanizo la Khoka
Amupeputsa Yesu ku Nazareti
Kuphedwa kwa Yohane Mʼbatizi
Yesu Adyetsa Anthu 5,000
Yesu Ayenda pa Nyanja
Miyambo ya Makolo
Mayi wa ku Kanaani
Yesu Adyetsa Anthu 4,000
Afarisi ndi Asaduki Afuna Chizindikiro
Yisiti wa Afarisi ndi Asaduki
Petro Avomereza za Yesu
Yesu Aneneratu za Imfa Yake
Za Kusenza Mtanda
Maonekedwe Aulemerero a Yesu pa Phiri
Yesu Achiritsa Wodwala Matenda Akugwa
Yesu Anena za Imfa yake Kachiwiri
Yesu Apereka Msonkho
Wamkulu mu Ufumu Wakumwamba
Za Kuchimwitsa Ena
Fanizo la Nkhosa Yotayika
Za Mʼbale Amene Akuchimwirani
Fanizo la Wantchito Wopanda Chifundo
Za Kuthetsa Ukwati
Yesu Adalitsa Ana
Mnyamata Wolemera ndi Ufumu wa Mulungu
Fanizo la Aganyu Mʼmunda wa Mphesa
Yesu Anenanso za Imfa Yake
Pempho la Mkazi wa Zebedayo
Yesu Achiritsa Anthu Awiri Osaona
Yesu Alowa mu Yerusalemu
Yesu mʼNyumba ya Mulungu
Yesu Atemberera Mtengo wa Mkuyu
Amufunsa Yesu za Ulamuliro Wake
Fanizo la Ana Amuna Awiri
Fanizo la Alimi
Fanizo la Phwando la Ukwati
Za Kupereka Msonkho
Ukwati ndi za Kuuka kwa Akufa
Lamulo Lalikulu Koposa
Kodi Khristu ndi Mwana wa Ndani?
Yesu Adzudzula Aphunzitsi Amalamulo ndi Afarisi
Tsoka kwa Aphunzitsi Amalamulo ndi Afarisi
Zizindikiro za Masiku Otsiriza
Tsiku ndi Nthawi Sizidziwika
Wantchito Wokhulupirika ndi Wosakhulupirika
Fanizo la Anamwali Khumi
Fanizo la Kagwiritsidwe Ntchito ka Ndalama
Nkhosa ndi Mbuzi
Chiwembu cha Ayuda pa Yesu
Yesu Adzozedwa ku Betaniya
Yudasi Avomereza Kupereka Yesu
Paska Womaliza ndi Mgonero wa Ambuye
Yesu Aneneratu kuti Petro Adzamukana
Yesu mu Getsemani
Amugwira Yesu
Yesu ku Bwalo la Akulu Ayuda
Petro Amukana Yesu
Yudasi Adzimangirira
Yesu kwa Pilato
Asilikali Amuchita Chipongwe Yesu
Amupachika Yesu
Kufa kwa Yesu
Yesu Ayikidwa Mʼmanda
Alonda a pa Manda
Yesu Auka kwa Akufa
Uthenga wa Alonda
Yesu Atuma Ophunzira Ake