^
MASALIMO
BUKU LOYAMBA
Salimo la Davide. Atathawa mwana wake Abisalomu.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe wa zida za zingwe. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe zoyimbira za zitoliro. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Molingana ndi seminiti. Salimo la Davide.
Sigioni wa Davide, amene anayimbira Yehova zokhudza Kusi, wa fuko la Benjamini.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa gititi. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe a nyimbo ya “Imfa ya Mwana.” Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe seminiti. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
Salimo la Davide.
Mikitamu ya Davide.
Pemphero la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide mtumiki wa Yehova. Iye anayimbira Yehova nyimbo iyi pamene Yehovayo anamupulumutsa mʼdzanja la adani ake onse ndiponso mʼdzanja la Sauli.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa “Mbawala yayikazi ya Mmawa.” Salimo la Davide.
Salimo la Davide.
Salimo la Davide.
Salimo la Davide.
Salimo la Davide.
Salimo la Davide.
Salimo la Davide.
Salimo la Davide.
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba popereka Nyumba ya Mulungu.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
Salimo la Davide. Malangizo.
Salimo la Davide. Pamene iye ananyengezera misala pamaso pa Abimeleki, amene anamupirikitsa, iyeyo nʼkuchoka.
Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide, mtumiki wa Yehova.
Salimo la Davide.
Salimo la Davide. Kupempha.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Kwa Yedutuni. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
BUKU LACHIWIRI
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Ndakatulo ya ana a Kora.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Ndakatulo ya ana a Kora.
Kwa mtsogoleri wamayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe a “Maluwa a Kakombo.” Salimo la ana a Kora. Nyimbo ya pa ukwati.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Ndakatulo ya ana a Kora. Nyimbo ya anamwali.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la ana a Kora.
Nyimbo. Salimo la ana a Kora.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la ana a Kora.
Salimo la Asafu.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pamene Mneneri Natani anabwera kwa iye atachita chigololo ndi Batiseba.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe, ndakatulo ya Davide; pamene Doegi Mwedomu anapita kwa Sauli ndi kunena kuti “Davide wapita ku nyumba ya Ahimeleki.”
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a Mahalati. Ndakatulo ya Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Ndakatulo ya Davide. Pamene anthu a ku Zifi anapita kwa Sauli ndipo anati, “Kodi Davide sakubisala pakati pathu.”
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Ndakatulo ya Davide. Pa zoyimbira za zingwe.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Njiwa pa Mtengo wa Thundu wa Kutali.” Mikitamu ya Davide, pamene Afilisti anamugwira ku Gati.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Ndakatulo ya Davide, pamene anathawa Sauli kupita ku phanga.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Ndakatulo ya Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Ndakatulo ya Davide. Pamene Sauli anatumiza anthu kuti akalondere nyumba ya Davide ndi cholinga choti amuphe.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Kakombo wa Pangano.” Mikitamu ya Davide yophunzitsira. Pamene anamenyana ndi Mesopotamiya ndi Aramu-Zoba, ndi pamene Yowabu anabwerera ndi kukantha Aedomu 12,000 mʼChigwa cha Mchere.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Loyimbidwa ndi zipangizo za zingwe.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Kutsata mayimbidwe a Yedutuni. Salimo la Davide.
Salimo la Davide. Pamene anali mʼchipululu cha Yuda.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Nyimbo.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Potsata mayimbidwe a “Akakombo.”
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho.
Salimo la Solomoni.
BUKU LACHITATU
Salimo la Asafu.
Ndakatulo ya Asafu.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe, potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Salimo la Asafu. Nyimbo.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo la Asafu.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a Yedutuni. Salimo la Asafu.
Ndakatulo ya Asafu.
Salimo la Asafu.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Kakombo wa Pangano.” Salimo la Asafu.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a gititi. Salimo la Asafu.
Salimo la Asafu.
Nyimbo. Salimo la Asafu.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a Gititi. Salimo la ana a Kora.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la ana a Kora.
Pemphero la Davide.
Salimo la Ana a Kora.
Salimo la ana a Kora. Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a nyimbo yoti: “Pa Matenda ndi pa Mazunzo.” Ndakatulo ya Hemani, wa banja la Ezara.
Ndakatulo ya Etani, wa banja la Ezara.
BUKU LACHINAYI
Pemphero la Mose munthu wa Mulungu.
Salimo. Nyimbo ya pa tsiku la Sabata.
Salimo.
Salimo. Nyimbo yothokoza.
Salimo la Davide.
Pemphero la munthu wosautsidwa, pamene walefuka, nakhuthulira pamaso pa Yehova kulira kwakeko.
Salimo la Davide.
BUKU LACHISANU
Nyimbo. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wamayimbidwe. Salimo la Davide.
Salimo la Davide.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Solomoni.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
Salimo la Davide.
Ndakatulo ya Davide, pamene iyeyo anali mʼphanga. Pemphero.
Salimo la Davide.
Salimo la Davide.
Salimo la matamando la Davide.