^
GENESIS
Chiyambi cha Chilengedwe
Adamu ndi Hava
Kuchimwa kwa Munthu
Kaini ndi Abele
Banja la Kaini
Mibado Kuyambira pa Adamu Mpaka Nowa
Kuyipa kwa Mtundu wa Anthu
Nowa ndi Chigumula
Nowa Atuluka Mʼchombo
Pangano la Mulungu ndi Nowa
Ana Aamuna a Nowa
Mndandanda wa Mitundu ya Anthu
Banja la Yafeti
Banja la Hamu
Banja la Semu
Nsanja ya Babeli
Mibado Kuyambira pa Semu Mpaka Abramu
Mibado Yochokera mwa Tera
Mulungu Ayitana Abramu
Abramu ku Igupto
Abramu Asiyana ndi Loti
Abramu Apulumutsa Loti
Pangano la Mulungu ndi Abramu
Sarai ndi Hagara
Pangano la Mdulidwe
Alendo Atatu a Abrahamu
Abrahamu Apembedzera Sodomu
Kuwonongedwa kwa Sodomu ndi Gomora
Loti ndi Ana ake Aakazi
Abrahamu ndi Mfumu Abimeleki
Kubadwa kwa Isake
Kuchotsedwa kwa Hagara ndi Ismaeli
Pangano la ku Beeriseba
Kuyesedwa kwa Abrahamu
Ana Aamuna a Nahori
Kumwalira kwa Sara
Isake ndi Rebeka
Abrahamu Amwalira
Ana Aamuna a Ismaeli
Yakobo ndi Esau
Isake ndi Abimeleki
Yakobo Alandira Madalitso kwa Isake
Yakobo Athawira kwa Labani
Maloto a Yakobo pa Beteli
Yakobo Afika ku Padanaramu
Yakobo Akwatira Leya ndi Rakele
Ana a Yakobo
Nkhosa za Yakobo Zichuluka
Yakobo Athawa Labani
Labani Alondola Yakobo
Yakobo Akonzekera Kukumana ndi Esau
Yakobo Alimbana ndi Mulungu
Yakobo Akumana ndi Esau
Dina ndi Sekemu
Yakobo Abwerera ku Beteli
Imfa ya Isake ndi Rakele
Zidzukulu za Esau
Mafumu a ku Edomu
Maloto a Yosefe
Yosefe Agulitsidwa ndi Abale Ake
Yuda ndi Tamara
Yosefe ndi Mkazi wa Potifara
Yosefe Amasulira Maloto a Amʼndende Anzake
Maloto a Farao
Yosefe Alamulira Dziko la Igupto
Abale a Yosefe Apita ku Igupto
Ulendo Wachiwiri wa ku Igupto
Chikho Chasiliva Mʼthumba la Benjamini
Yosefe Adziwulula kwa Abale Ake
Yakobo Apita ku Igupto
Yosefe pa Nthawi ya Njala
Manase ndi Efereimu
Yakobo Adalitsa Ana ake Aamuna
Kumwalira kwa Yakobo
Yosefe Abwereza Kutsimikizira Abale Ake
Kumwalira kwa Yosefe